9 months ago
9 months ago
Sunday Morning Verse [ Yesaya 4:1 ]
Tsiku limenelo akazi asanu ndi awiri adzagwira mwamuna mmodzi,
nʼkunena kuti, “Ife tizidya chakudya chathuchathu,
ndi kuvala zovala zathu;
inu mungotilola kuti tidziyitanidwa ndi dzina lanu.
Tichotseni manyazi aumbeta!”
GOODMORNING ☀️
Tsiku limenelo akazi asanu ndi awiri adzagwira mwamuna mmodzi,
nʼkunena kuti, “Ife tizidya chakudya chathuchathu,
ndi kuvala zovala zathu;
inu mungotilola kuti tidziyitanidwa ndi dzina lanu.
Tichotseni manyazi aumbeta!”
GOODMORNING ☀️
9 months ago
Kulowa Mkati Sikudali Kophweka. Welcome to Maula Prison Movie yatsala pang’ono kuonetsedwa 🍿
[ 📷 Amuna Achisale ali mkati ]
[ 📷 Amuna Achisale ali mkati ]
9 months ago
9 months ago
NO TIME FI WASTE-: Newly signed artist under porch time records, Oana will drop her first song under the label this Monday.
9 months ago
Onesimus One Man Concert Official Set List is Out 🎙️
Usiku uno ku Capetown, African ******* er akaswa nyimbo 20 izi Nonstop
Usiku uno ku Capetown, African ******* er akaswa nyimbo 20 izi Nonstop
9 months ago
Team ya Welcome to Maula Prison tsopano ili mu Blantyre ndipo usiku uno ntchito ilipo ku Mount Soche 🎥
9 months ago
Happy 25th Anniversary to Pastor Steven and Pastor Zipporah ( Founders of Zipporah International Foundation ).
Dzaka 25 ali limodzi. Chinsinsi chawo chili pati ?
25th Silver Jubilee Anniversary
Dzaka 25 ali limodzi. Chinsinsi chawo chili pati ?
25th Silver Jubilee Anniversary
9 months ago
Nachimalaya Namadingo, Temwa, Beejay & Ace ****** y, Joe Ikon, Crispy Mw, SlyC , and Sean Morgan are ready and set to perform at the MO626 intercollege show happening at Luanar ( Bunda Campus ) tonight !
9 months ago
“ Amene munapita ku Premiere sikuti muyambe kutifokozela m’mene zinalili. Mukambilane konko ndipo mutisiye apa YouTube Nafe tidzakambilana “ - Anthu M'ma Group 🍿
9 months ago
Mwanayu tu si AJuh Koma Zeze. Uyu adali producer mu studio mwa Daredevilz. Ma artist akulu akulu onsewa, Zeze ankawapanga record, GD ******* ixer ma vocals, uku Marcus ma instrumental.
Nkhani ya Zeze ukayimva, ngati sewero la tikufelanji
Nkhani ya Zeze ukayimva, ngati sewero la tikufelanji
9 months ago
Movie yatha ndipo anthu ayamika kuti ntchito yagwilidwa. Mawa ku Mount Soche ndipo Sunday ku Mzuzu 👏👏👏 Ena idzatipeza pa yuchubu
9 months ago
Aka nkoyamba AJuh kufika 100K views in 1 Day. Congratulations mwana iwe AJuh guffi 👏
Ili pa repeat https://youtu.be/oi2EPa_E2...
Ili pa repeat https://youtu.be/oi2EPa_E2...
9 months ago
Phalombe Sweetness yafika pa Theba 🇿🇦
Atsikana omwe abhebhesa ntchito zaku bedi mma banja 'Tomaida and Marcelline' akuziwisa aMalawi kujoni kuti pakadali pano ali ku Capetown ndipo sunday apezekela ku Jo'burg. Kwa amene afuna kulumikizana nawo ******* kuwayimbila pa +27754842655
Atsikana omwe abhebhesa ntchito zaku bedi mma banja 'Tomaida and Marcelline' akuziwisa aMalawi kujoni kuti pakadali pano ali ku Capetown ndipo sunday apezekela ku Jo'burg. Kwa amene afuna kulumikizana nawo ******* kuwayimbila pa +27754842655
9 months ago
9 months ago
‘HOW TO MAKE MONEY GROW ON TREES’ 📕
👆🏽 ili ndi Buku latsopano limene walemba Tendai Shaba ndipo latuluka
Pofokotokoza za zimene zili mu buku li, iye adalankhula mchizungu nati “ We’re still behind on educating our hardworking Malawians about financial literacy and personal finance. This book is all about how we can grow the little we make “ - Watero International Author, Tendai
Buku lo likupezeka apa https://shorturl.at/WJofC
👆🏽 ili ndi Buku latsopano limene walemba Tendai Shaba ndipo latuluka
Pofokotokoza za zimene zili mu buku li, iye adalankhula mchizungu nati “ We’re still behind on educating our hardworking Malawians about financial literacy and personal finance. This book is all about how we can grow the little we make “ - Watero International Author, Tendai
Buku lo likupezeka apa https://shorturl.at/WJofC
9 months ago
Kulowa Mkati Sikudali Kophweka. Welcome to Maula Prison Movie yatsala pang’ono kuonetsedwa 🍿
[ 📷 Amuna Achisale ali mkati ]
[ 📷 Amuna Achisale ali mkati ]
9 months ago
“ The people I call my parents today aren’t my biological parents. They adopted me and have raised me for over 20 years. They are the Mundias and I am Mulenga “ - Zambian superstar, Yo Maps reveals
Yo Maps says he never saw his biological Dad who died while he was still a baby. His mother later died while he was very young. That’s when he was adopted by the Mundias.
Akati Mwana wa Mzako ndi Wako emwe. Lero makolo awa waamangila ma mansion
Yo Maps says he never saw his biological Dad who died while he was still a baby. His mother later died while he was very young. That’s when he was adopted by the Mundias.
Akati Mwana wa Mzako ndi Wako emwe. Lero makolo awa waamangila ma mansion
Sponsored by
Comfort
4 months ago